Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Chakwera ayendera chitukuko cha mphepete mwa nyanja ku Mangochi

Mtsogoleri wadziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akuyendera ntchito zosiyanasiyana zachitukuko m’boma la Mangochi.

Kuchoka apo, Dr Chakwera ayendera ntchito yomanga ofesi yatsopano ku khonsolo ya Mangochi, ntchito yomwe boma likugwira mogwirizana ndi dziko la Iceland.

Kenako, Dr Chakwera afika ku Monkey Bay, kumene ayenderenso ntchito ya msewu wa Monkey Bay – Cape Maclear- T378 mdera la mfumu yaikulu Nankumba.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

‘Sankhani moyenera zokaphunzira ku university’

MBC Online

PRISAM, MARANATHA ACADEMY OFFER FULL SCHOLARSHIP TO BRIGHT NEEDY STUDENT

McDonald Chiwayula

RA, Stakeholders to relocate Muloza One Stop Border Post

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.