Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Khonsolo ya mnzinda wa Zomba ili ndi Mfumu yatsopano

Khonsolo ya mnzinda wa Zomba yasankha a Christopher Jana adera la Mpira ngati mfumu yatsopano ya mnzindawu.

A Jana alowa mmalo mwa a Davie Maunde omwe akhala pa mpandowu kuchoka chaka cha 2021 atasankhidwa mmwezi wa December mchakacho.

A Anthony Gonani ndiye wachiwiri kulowa mmalo mwa a Munira Bakali a Likangala ward.

A Jana anakhalaponso pa udindowu mchaka cha 2018 kufika 2020 pomwe khansala Benson Bula anatenga udindowu kufikira 2021.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

MBC yati Kapusa anali katakwe

Blessings Kanache

Malawi Fertilizer Company itha kupanga fertilizer okwana 150, 000 tons

MBC Online

Bambo alamulidwa agwire jere kwa zaka 12 atagwilira

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.