Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

‘Dziko la Mozambique ndi lofunika pa chitukoko chathu’

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wati aMalawi akuyenera kugwira ntchito molimbikira kuti dziko lino lipeze chuma.

Dr Chakwera ati zina mwa ntchito zimene zikugwiridwa m’dziko lino zikutheka kaamba kaubale wabwino umene ulipo pakati pa dziko la Malawi ndi la Mozambique, kudzera mwa mtsogoleri wa dzikolo, Dr Filipe Jacinto Nyusi.

Dr Chakwera atinso kudzera mu ulimi, dziko lino litukuka maka likatsatira njira zamakono zaulimi.

Iye amayankhula potsekulira chionetsero cha malonda a zaulimi, pamodzi ndi Dr Nyusi, mu mzinda wa Blantyre.

Related posts

French energy company donates solar system to Mangochi Orphans and Education Training School

McDonald Chiwayula

Tabitha wins Golden Boot

Romeo Umali

Blue Eagles yayamba moyo wa ligi ya Chipiku ndichipambano

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.