Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Religion

Dr Chakwera akumana ndi atsogoleri azipembedzo

Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera m’mawa uno akuyembekezeka kukumana ndi atsogoleri azipembedzo zosiyanasiyana ku nyumba ya boma ya Chikoko Bay m’boma la Mangochi.

Pakadali pano, atsogoleri oyimira zipembedzo ayamba kufika ku zokambilanazi.

Dr Chakwera ali m’chigawo cha kummawa kumene akugwira ntchito zosiyanasiyana za boma.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

CGIAR donates K513 million equipment to boost Malawi’s food security

McDonald Chiwayula

MALAWI INVESTMENT FORUM UNDERWAY IN SOUTH AFRICA

Mayeso Chikhadzula

‘Mangani ofesi zoti anthu awulumali apeze thandizo mosavuta’

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.