Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Religion

Dr Chakwera akumana ndi atsogoleri azipembedzo

Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera m’mawa uno akuyembekezeka kukumana ndi atsogoleri azipembedzo zosiyanasiyana ku nyumba ya boma ya Chikoko Bay m’boma la Mangochi.

Pakadali pano, atsogoleri oyimira zipembedzo ayamba kufika ku zokambilanazi.

Dr Chakwera ali m’chigawo cha kummawa kumene akugwira ntchito zosiyanasiyana za boma.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Ntchisi youths empowered through tailoring

Rabson Kondowe

Mediation efforts to end truck drivers’ strike underway

MBC Online

International Blantyre Cancer Centre Inaugurated

Secret Segula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.