Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Chakwera Wathokoza Livingstonia Synod

President Dr Lazarus Chakwera wathokoza Sinodi ya Livingstonia ya mpingo wa CCAP chifukwa chothandiza boma pa ntchito zosiyanasiyana za chitukuko.

Poyankhula pa mwambo wa mapemphero womwe ukuchitika pa mpingo wa Mchengautuba ku Mzuzu, a Chakwera ayamikira kuti sinodi ikuthandiza mu nthambi za maphunziro, ukhondo komanso kuthetsa njala m’dziko muno.

Iye wati ichi ndi chizindikiro chakuti mpingowu ndi wodzipereka pofuna kuonetsetsa kuti masomphenya a dziko lino a mlozo wa 2063 akwanilitsidwa.

Related posts

Ndende zisintha – Boma

Rabson Kondowe

Mbava ipempha chilango chofewa chifukwa anayigulula mano

Rabson Kondowe

Asiya zolemba, akufuna ku nyumba ya malamulo

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.