Malawi Broadcasting Corporation
Africa Local News Nkhani Sports Sports

MUSALOLE ANA KUCHITA JUGA – MAGLA

Bungwe la Malawi Gaming and Lotteries Authority ( MAGLA), lachenjeza kuti lamulo ligwira ntchito kwa makolo omwe amalimbikitsa ana awo kuchita juga.

Mkulu wa bungwe la MAGLA a Rachel Mijiga ati ndi kuphwanya malamulo kulola mwana ochepera zakha 18 kuchita nawo masewero-wa.

A Mijiga amafotokoza izi lachisanu, pa mwambo obzyala mitengo mu mzinda wa Lilongwe.

Bungwe la MAGLA ndi bungwe lomwe limaonetsetsa kuti anthu komanso makampane azitsatira malamulo a juga.

Olemba:  Tasungana Kazembe.

Related posts

Remnant Lions Theatre Group to premier “Belinda”

Rabson Kondowe

Malawi, others in joint football tournament

Romeo Umali

NBM for accurate, empowered media – Hiwa

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.