Malawi Broadcasting Corporation
Africa Local News Nkhani Sports Sports

MUSALOLE ANA KUCHITA JUGA – MAGLA

Bungwe la Malawi Gaming and Lotteries Authority ( MAGLA), lachenjeza kuti lamulo ligwira ntchito kwa makolo omwe amalimbikitsa ana awo kuchita juga.

Mkulu wa bungwe la MAGLA a Rachel Mijiga ati ndi kuphwanya malamulo kulola mwana ochepera zakha 18 kuchita nawo masewero-wa.

A Mijiga amafotokoza izi lachisanu, pa mwambo obzyala mitengo mu mzinda wa Lilongwe.

Bungwe la MAGLA ndi bungwe lomwe limaonetsetsa kuti anthu komanso makampane azitsatira malamulo a juga.

Olemba:  Tasungana Kazembe.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

National competition authorities hailed for protecting consumer rights

MBC Online

Gulu la alimi lapeza K620 million kudzera mu ulimi wa nzimbe

Doreen Sonani

Unduna wa za umoyo ndi okhudzidwa ndi kuchuluka kwa matenda a mu ubongo

Beatrice Mwape
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.