Amene akonza phwando la mayimbidwe la Ku Mingoli Bash achotsa oyimba onse akunja monga Cassper Nyovest ndi Young Stunna pam’ndandanda wa oimba akuphwando la chaka...
Anthu amunzinda wa Blantyre anali okondwa kwambiri ataonelera maimbidwe ochititsa chidwi kuchoka kwa oimba wa chamba cha amapiano, Young Stunna, wochokera m’dziko la South Africa....
Oyimba nyimbo za uzimu ati ndi okondwa ndi momwe nzika za mu nzinda wa Lilongwe zinabwelera pa phwando la maimbidwe limene linachitikira ku Sheaffer lolemba...
Katswiri oyimba amene amachokera m’boma la Phalombe, Giboh Pearson, wapulumuka pa ngozi ya galimoto yomwe wachita pomwe amapita ku phwando la msangulutso ku Bangwe mu...
Mwambo wa maliro a Hope Chisanu wayamba tsopano kumudzi kwa Nyaka, mdera la Mfumu Kalumbu ku Lilongwe. Polankhula pa mwambowo, Msuweni wa Hope Chisanu wathokoza...
Church funeral service for veteran actor and broadcaster late Hope Chisanu is underway at Presbyterian Church of Malawi (PCM) in Lilongwe where he used to...
Charles Sinetre ndimmodzi wa akatswiri amene adayimba limodzi ndi malemu Lucius Banda. Kodi adzamukumbukira motani? Olembankhani wathu Simeon Boyce anacheza ndi Sinetre motere: Q-Kodi ndi...
Yemwe amakhala pafupi ndi nyumba ya malemu “soldier” Lucius Banda m’boma la Balaka, Ras Jonah, yemwe dzina lake lenileni ndi Ronald Chigwale, wati mu nyimbo...
President Dr Lazarus Chakwera has paid tribute to legendary artist ‘soldier’ Lucius Banda, who before his demise on Sunday served as the Presidential Advisor on...
Journalist and author Herbert Katanda intends to launch a book titled The Audacity of Depression on Saturday in Lilongwe as part of his contributions to...