Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Anthu apitilira kukhuza maliro a bambo Kapusa

Nduna yoona za madzi komanso ukhondo, mayi Abida Mia, pamodzi ndi anthu ena ambiri, asonkhana ku Machinjiri Area 3 mu mzinda wa Blantyre kumene akukhuza maliro a bambo Geoffrey Kapusa.

Malemu Kapusa anali m’modzi wa anthu odziwika bwino poulutsa mawu ndipo anadziwika ndi programme yotchedwa ‘Music Splash’ pa kanema wa MBC m’zaka zapitazo.

Kumene kuli zovutaku kukhala mwambo wa mapemphero kenako maliro anyamulidwa kupita ku mudzi wa Mkanda ku Malosa m’boma la Zomba komwe akawayike m’manda lachinayi.

Iwo amwalira m’banda kucha wa lero pa chipatala cha Queen Elizabeth.

#MBCDigital
#Manthu

Related posts

Malemu Kayanula anali Mlangizi

Romeo Umali

Wobera anthu m’magalimoto amugamula zaka zitatu kundende

Rabson Kondowe

Kanengo Police takes crime fight to the pulpit

Yamikani Simtowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.