Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Chakwera akhala nawo pa mapemphero a misa

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera pamodzi ndi mayi wa fuko lino Madam Monica Chakwera akuyembekezeka kukhala nawo pa mapemphero a misa pa mpingo wa katolika wa St. Peters mu mzinda wa Mzuzu.

Mtsogoleri wa dziko linoyu akuyembekezeka kufika pa mpingowu cha m’ma 10 koloko m’mawa uno.

Olemba: Jackson Sichali.

 

Related posts

IMPALA Patient Monitor poised to transform pediatric healthcare in Africa

Rabson Kondowe

NEW SELF- CHARGING ELECTRIC VEHICLE TO HIT THE AFRICAN MARKET SOON

MBC Online

Chakwera to arrive in BT

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.