Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Chakwera akhala nawo pa Misa ya mayi Shanil Dzimbiri

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr.Lazrus Chakwera, akhala nawo pamwambo wa nsembe ya Misa ya mayi Shanil Dzimbiri kunyumba ya chisoni ya Sunrise ku Kanengo munzinda wa Lilongwe.

Mayi Dzimbiri m’mbuyomu anali anali mkazi wa mtsogoleri wakale wa dziko lino, Bakili Muluzi, ndipo mwambowu ndiwoperekeza thupi lawo kumudzi kwawo ku Balaka komwe akuyembekezeka kukayikidwa mmanda mawa pa 14 June.

Atsogoleri akale adziko lino Dr.Bakili Muluzi komanso Dr.Joyce Banda ndi Retired Chief Justice Richard Banda afika kale, kuphatikizapo ana amalemu Shanil ndi nduna zambiri zaboma ndi akuluakulu ena.

By Mirriam Kaliza

Related posts

MMCL launches multi-million cannabis processing plant project

Rabson Kondowe

February registers a 58% rise in share value on MSE

Rabson Kondowe

Flames yakale isewera ndi Zambia yakale

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.