Malawi Broadcasting Corporation
International News Nkhani

Mohammad Mokhber ndi mtsogoleri wa dziko la Iran

Wachiwiri kwa Mtsogoleri wa dziko la Iran a Mohammad Mokhber nde mtsogoleri watsopano wa dzikoli kutsatira imfa ya mtsogoleri wawo a Ebrahim Raisi pa ngozi ya ndege.

Malinga ndi gawo 131 la malamulo oyendetsera dzikoli, a Mokhber akuyenera kugwira ntchito ndi akulu akulu a nyumba ya malamulo komanso akulu akulu owona malamulo pokonzekera chisankho cha President chomwe chichitike m’masiku osapyola makumi asanu.

 

Related posts

‘Nduna yayikulu ku UK idzigula yokha zovala, magalasi a maso’

Romeo Umali

A Chakwera acheza ndi ochita malonda kunyumba ya boma

Rabson Kondowe

Owona zaumoyo atulutsa zotsatira zonse za ‘ambuye tengeni’ mu sabata ziwiri

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.