Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Sports Sports

Bullets ichita mdipiti ku Blantyre

Timu ya FCB Nyasa Big Bullets lero ili ndi mdipiti (Street Parade) mumzinda wa Blantyre pomwe, mwazina, akusonyeza zikho zimene timuyi inaanyamula mu season yapitayi.

Malinga ndi mlembi wamkulu wakomiti yamasapota a timuyi, Archibald Kasakura, cholinga chake ndi kuthokoza masapota onse chifukwa choyichemelera timuyi komanso bank ya FCB chifukwa cha thandizo lake.

Ulendowu wayambira pa Kamuzu Upper Stadium kudutsa mu Masauko Chipembere Highway mpaka kukafika mkatikati mwa Blantyre ndipo ukathera ku Ndirande.

#MBCOnlineServices

Related posts

Six Super League teams adhere to Football Coaches Association’s minimum wage standard

Rabson Kondowe

Progress in Human-Wildlife Conflict Reduction Reported by Tourism Ministry

Rabson Kondowe

Msonkhano waukulu tichita mu September — JB

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.