Malawi Broadcasting Corporation
Environment Local Local News Nkhani

MVULA YABWERANSO

Nthambi yowona za nyengo m’dziko muno yati mvula ikhala ikugwa mpakana sabata ya mawa, pamene yayamba kuvumba m’maboma ambiri kuyambira loweruka m’mawa.

Ena ati zimenezi zitha kupangitsa kuti mbewu zosiyanasiyana, zimene zinayamba kunyala chifukwa cha ng’amba, zitsitsimuke pamene mvula yagwa.

Kubwera kwa mvulaku kwaika chikhulupiliro mea ambiri kuti mwina alimi akhoza kukolora mokwanira, zimene zingathandize kupewa njala.

Related posts

Sunbird Hotels pumps K5million to Presidential Golf tourney

Rabson Kondowe

CAMA in favour of fuel price hike

Romeo Umali

Self-help initiatives springing up in Mwanza

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.