Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

Sitima ya Marka itha kufika — Chithyola Banda

Sitima yochekera ku Beira m’dziko la Mozambique itha kufika ku Marka m’boma la Nsanje, atero a Chithyola Banda.

Nduna ya zachuma yi yatsindika kuti ntchito yokonza njanji ya sitima kuchoka ku Marka kufika ku Bangula yafika pamapeto, ndipo sitima itha kufika kuchoka ku Beira.

Iwo ayi izi zithandiza kupititsa chuma cha dziko lino patsogolo, maka kupyolera mu ntchito za malonda.

Related posts

Kambira Secondary School opened

MBC Online

Dedza stands united as they mourn former VP

Romeo Umali

Chakwera condemns corruption in developmental initiatives

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.