Alimi ambiri a fodya akupitilira kusangalala ndi mitengo yabwino yomwe kampani zogula fodya zikupereka kwa alimiwa kumisika. Malinga ndi a Musaiwale Kavina, amene ndi mmodzi...
Katswiri wankhonya Limbani Masamba wabweza chipongwe chomwe adachitiridwa ndi Simeon Tcheta chaka chatha pomugonjetsa kudzera pa ma points pa nkhonya ya mtima bii yomwe inali...
Patrick Mabedi, coach of the Malawi National Football Team, has released his final squad for the matches against São Tomé and Príncipe and Equatorial Guinea....
Phungu wa Dera la Nsanje Lalanje, wayamikira boma pobweretsa chitukuko cha nyumba ya ma kompyuta pa sukulu ya Phokela CDSS mderalo. Phunguyi, a Gladys Ganda,...
Malawi Congress Party (MCP) Director of Youth, Richard Chimwendo Banda, has emphasized that President Lazarus Chakwera is committed to ensuring that development projects reach all...
Timu ya Silver Strikers idakali patsogolo pa m’ndandanda wa matimu amu TNM Super League itagonjetsa timu ya FCB Nyasa Big Bullets 1-0 Lamulungu pa bwalo...
Mulhoko wamphirameto wa FCB Nyasa Big Bullets wookelhemulhiwa ni Silver Strikers vamatheelha ayo yeereyelha va Kamuzu Stadium o Blantyre. Chinsisi Maonga amulhoko wa Silver Strikers...
Amaryllis Hotel General Manager Ramy Waheed has encouraged Malawian youths to unleash their innovative potential and develop ideas that align with the Malawi 2063. Waheed...
Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Saulos Chilima tsopano wafika m’dziko la Republic of Korea kumene akachite nawo msonkhano waukulu pakati pa dzikolo ndi...