Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News Nkhani

Msonkho pa ma belo wabwerera kuzakale

Mkulu wabungwe lotolera misonkho, a John Biziwick, walamula kuti ogwira ntchito kubungweli aleke kugwiritsa ntchito msonkho okwera pa mabelo a zovala, umene anaukhazikitsa posachedwapa.

Izi zikudza patangodutsa nthawi yochepa ochita malonda amtunduwu munzinda wa Lilongwe atachita zionetsero ndikukapereka madandaulo awo ku ofesi za bungweli.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

CHAKWERA CALLS FOR HARD WORK AMONG MALAWIANS

McDonald Chiwayula

Govt to strengthen labour sector

Arthur Chokhotho

Ex-convicts arrested for suspected burglary

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.