Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Usi ali ku khonsolo ya Thyolo

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, afika ku ofesi ya Bwanamkubwa wa boma la Thyolo pa ulendo wawo oyendera ntchito za boma mwadzidzidzi.

Iwo afika nthawi itangokwana kota pasiti seveni (7:15) m’mawa uno.

Pakadali pano, DC wa boma la Thyolo, a Hudson Kuphanga, akufotokozera a Usi ntchito zomwe zikugwiridwa m’bomalo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Malawi Beach Soccer delays departure for AFCON Qualifier

Romeo Umali

CHAKWERA MALAWI BOUND

Blessings Kanache

Silver Strikers clinch TNM Super League title

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.