Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Usi ali ku khonsolo ya Thyolo

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, afika ku ofesi ya Bwanamkubwa wa boma la Thyolo pa ulendo wawo oyendera ntchito za boma mwadzidzidzi.

Iwo afika nthawi itangokwana kota pasiti seveni (7:15) m’mawa uno.

Pakadali pano, DC wa boma la Thyolo, a Hudson Kuphanga, akufotokozera a Usi ntchito zomwe zikugwiridwa m’bomalo.

 

Related posts

Chakwera to officiate private sector agriculture mechanisation

Blessings Kanache

Veterinary surgeon calls for certified rabies vaccination

Rabson Kondowe

Benylin Paediatric Cough Syrup recalled in COMESA Region

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.