Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Usi ali ku khonsolo ya Thyolo

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, afika ku ofesi ya Bwanamkubwa wa boma la Thyolo pa ulendo wawo oyendera ntchito za boma mwadzidzidzi.

Iwo afika nthawi itangokwana kota pasiti seveni (7:15) m’mawa uno.

Pakadali pano, DC wa boma la Thyolo, a Hudson Kuphanga, akufotokozera a Usi ntchito zomwe zikugwiridwa m’bomalo.

 

Related posts

Afrox officials visit Malawi

Mayeso Chikhadzula

PDP commends MEC for fair conduct in by-elections

Rabson Kondowe

Self-upgraded teachers to compete in promotional interviews —Govt

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.