Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Dr Usi akhumudwa ndi kuonongwedwa kwa CDF

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi ati ndi okhumudwa kuti ena mwa aphungu anyumba ya malamulo sakuonetsa chidwi chogwiritsa ntchito ndalama zonse zomwe zili mu dongosolo la Community Development Fund (CDF).

Dr Usi amanena izi mu ofesi ya a Bwanamkubwa a m’boma la Thyolo a Hudson Kuphanga.

A Kaphanga amafotokoza kuti zina mwa ndalama zomwe aphunguwa amalandila m’madera a aphungu, sazimvetsa komanso samazigwiritsa ntchito zonse pa chitukuko.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Beneficiaries applaud govt for early distribution of maize

MBC Online

Sing’anga akakhala kundende pamlandu ogwililira

Charles Pensulo

FIRST LADY HAILS MUSLIM WORLD LEAGUE FOR PUMPING K8.5 BN FOR ORPHANS’ EDUCATION SUPPORT

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.