Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Dr Chakwera achita zokambilana zobweretsa sitima zapamadzi

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera akuyembekezeka kukambirana ndi kampani zoona za sitima zapamadzi ku Germany kuti athandize kuyambitsa ntchito za maulendo pa nyanja ya Malawi pothana ndi mavuto amayendedwe panyanjayi.

Nduna yoona nkhani zakunja a Nancy Tembo anena izi pomwe Dr Chakwera akuyembekezeka kufika ku Frankfurt ku Germany lachitatu kuchokera ku Italy komwe akakambilane ndi makampaniwa.

Iwo ati ali ku Germany, Dr Chakwera akambirana ndi kampaniyi za maulendowa poonjezela kukambirana zankhani ya magetsi asanakumane ndi mtsogoleri wa dziko la Germany.

Related posts

Abambo awiri awapeza olakwa pamulandu wosakaza nkhalango

Mayeso Chikhadzula

Kalembera wa chisankho cha makhansala sanaime, atero a MEC

Alinafe Mlamba

Chimbale chatsopano ndichothokoza Mulungu — Thuya

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.