Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Local Local News Nkhani

Zokonzekera za Ku Mingoli zili mkati

Zokonzekera zokhudza phwando la maimbidwe la Ku Mingoli zayambika pa bwalo la masewero la Civo mu mzinda wa Lilongwe pamene phwandoli lichitike loweluka likubwerali.

Khonsolo ya mzindawu nayo yachita mgwirizano ndi oyendetsa phwandoli pomwe masanawa mfumu ya mzindawu a Esther Sagawa anatsogolera ntchito yosesa malo ozungulira bwaloli.

Oimba oposa 21 a m’dziko muno ndi omwe adzayimbe patsikuli kufikira m’mawa wa tsiku Lamulungu.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

FMB Capital Holdings yapanga phindu lokwana K137.8 billion

Justin Mkweu

Petroleum importers provides safe water to Linyangwa Health Centre

Olive Phiri

Concern over illegal mining in Nkhotakota Game Reserve

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.