Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Local Local News Nkhani

Zokonzekera za Ku Mingoli zili mkati

Zokonzekera zokhudza phwando la maimbidwe la Ku Mingoli zayambika pa bwalo la masewero la Civo mu mzinda wa Lilongwe pamene phwandoli lichitike loweluka likubwerali.

Khonsolo ya mzindawu nayo yachita mgwirizano ndi oyendetsa phwandoli pomwe masanawa mfumu ya mzindawu a Esther Sagawa anatsogolera ntchito yosesa malo ozungulira bwaloli.

Oimba oposa 21 a m’dziko muno ndi omwe adzayimbe patsikuli kufikira m’mawa wa tsiku Lamulungu.

 

Related posts

MALAWI BROADCASTING CORPORATION EXECUTIVE MANAGEMENT PLACEMENT: DIRECTOR OF NEWS AND CURRENT AFFAIRS

McDonald Chiwayula

Khonsolo ya mzinda wa Lilongwe yagumula sitolo zoposa 60 mkatikati mwa Lilongwe

Rabson Kondowe

Govt launches cooperative leadership training

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.