Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Local Local News Nkhani

Zokonzekera za Ku Mingoli zili mkati

Zokonzekera zokhudza phwando la maimbidwe la Ku Mingoli zayambika pa bwalo la masewero la Civo mu mzinda wa Lilongwe pamene phwandoli lichitike loweluka likubwerali.

Khonsolo ya mzindawu nayo yachita mgwirizano ndi oyendetsa phwandoli pomwe masanawa mfumu ya mzindawu a Esther Sagawa anatsogolera ntchito yosesa malo ozungulira bwaloli.

Oimba oposa 21 a m’dziko muno ndi omwe adzayimbe patsikuli kufikira m’mawa wa tsiku Lamulungu.

 

Related posts

Govt, UNDP launch Africa Green Business and Financing Initiative Roadmap

Alinafe Mlamba

Wogwililira wapempha khoti kuti limukhululukire kaamba koti ndiwokalamba

Rabson Kondowe

Malawi makes strides on access to justice for women, girls

Doreen Sonani
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.