Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Local Local News Nkhani

Zokonzekera za Ku Mingoli zili mkati

Zokonzekera zokhudza phwando la maimbidwe la Ku Mingoli zayambika pa bwalo la masewero la Civo mu mzinda wa Lilongwe pamene phwandoli lichitike loweluka likubwerali.

Khonsolo ya mzindawu nayo yachita mgwirizano ndi oyendetsa phwandoli pomwe masanawa mfumu ya mzindawu a Esther Sagawa anatsogolera ntchito yosesa malo ozungulira bwaloli.

Oimba oposa 21 a m’dziko muno ndi omwe adzayimbe patsikuli kufikira m’mawa wa tsiku Lamulungu.

 

Related posts

MABEDI SPEAKS ON PERMANENT COACHING ROLE

MBC Online

Chilima returns from Seoul

Rabson Kondowe

E-payments in Mtukula Pakhomo excites beneficiaries

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.