Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Tikufufuzabe

Apolisi ku Limbe mu mzinda wa Blantyre ati akufufuzabe chifukwa chimene John Mwanamvekha, wazaka 26, wadziwombelera ndi mfuti.

Ofalitsankhani wapolisi ku Limbe, Aubrey Singanyama, wati izi zachitika loweruka ku Chigumula ku Blantyre.

Malinga ndi a Singanyama, John anadzitsekera mu galimoto asanadziombere.

Malemuyo anali wa m’mudzi wa Namathiya, mfumu yaikulu Mpunga m’boma la Chiradzulu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

WVM bails out hunger affected households in Chikwawa

Charles Pensulo

BUSHIRI BAILS OUT 65 NEEDY STUDENTS

MBC Online

CHAKWERA SENDS STRONG MESSAGE ON OPEN GOVERNANCE, CITIZEN ENGAGEMENT

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.