Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Tikufufuzabe

Apolisi ku Limbe mu mzinda wa Blantyre ati akufufuzabe chifukwa chimene John Mwanamvekha, wazaka 26, wadziwombelera ndi mfuti.

Ofalitsankhani wapolisi ku Limbe, Aubrey Singanyama, wati izi zachitika loweruka ku Chigumula ku Blantyre.

Malinga ndi a Singanyama, John anadzitsekera mu galimoto asanadziombere.

Malemuyo anali wa m’mudzi wa Namathiya, mfumu yaikulu Mpunga m’boma la Chiradzulu.

Related posts

PARLIAMENTARY COMMITTEE WORRIES WITH SMUGGLING

MBC Online

ArtGlo calls for collaboration against child abuse

Romeo Umali

Chilima leaves for the inaugural Korea – Africa summit

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.