Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Tikufufuzabe

Apolisi ku Limbe mu mzinda wa Blantyre ati akufufuzabe chifukwa chimene John Mwanamvekha, wazaka 26, wadziwombelera ndi mfuti.

Ofalitsankhani wapolisi ku Limbe, Aubrey Singanyama, wati izi zachitika loweruka ku Chigumula ku Blantyre.

Malinga ndi a Singanyama, John anadzitsekera mu galimoto asanadziombere.

Malemuyo anali wa m’mudzi wa Namathiya, mfumu yaikulu Mpunga m’boma la Chiradzulu.

Related posts

Opindula ndi Mtukula Pakhomo alandira dipo lawo pa lamya

Romeo Umali

Namibia sets the stage for Miss Teen and Miss Namibia 2025 Grand Finale

Steve Dakalira

CHAKWERA HAILS CULTURE AS PANACEA FOR UNITY

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.