Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local News Nkhani

Pulezidenti wakale wa FAMA wafunira zabwino Mayi Kingston

Mtsogoleri wakale wa bungwe la Film Association of Malawi (FAMA), a Gift Sukali, wafunira zabwino atsogoleri atsopano amene bungweli lawasankha kumene.

A Sukali ati ndi okondwa ndi kuti akuchoka pampandowu atakwaniritsa zambiri monga kuwonetsetsa kuti anthu akudziwa zazisudzo zapakanema komanso kutha kupeza phindu kupyolera mmakanemawa.

Iwo ati ali ndi chikhulupiliro kuti utsogoleri watsopanowu ukwaniritsa masomphenya a FAMA ndi kupititsa patsogolo bungweli kuti lithe kupeza thumba loliyendetsera.

Mtsogoleri watsopano wabungweli ndi a Dorothy Kingston, mkazi wa katswiri oyimba Zeze. Iwowa akhala akutsogolera bungweli kwa zaka zinayi.

 

Related posts

Mbayani Primary school wears a new face

Rabson Kondowe

Greenbelt Authority reaffirms commitment to compliance

MBC Online

DIGITALISATION KEY TO MALAWI 2063 ACTUALISATION – MACRA

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.