Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

President Chakwera akhala nawo pamwambo wa mapemphero

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akhala nawo pa mwambo wa mapemphero pa mpingo wa Monkey Bay Assemblies of God m’boma la Mangochi.

Mwambo wa mapemphero umenewu ukuyembekezeka kuyamba nthawi ya 9 koloko m’mawa uno.

President Chakwera ali m’chigawo chaku m’mawa kumene akugwira ntchito zaboma.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Minister of Mining warns against nepotism in maize flour distribution amidst growing food insecurity

Rabson Kondowe

MZUNI intensifies research

Romeo Umali

MBC 2ONTHEGO ON AZAM TV

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.