Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

President Chakwera akhala nawo pamwambo wa mapemphero

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akhala nawo pa mwambo wa mapemphero pa mpingo wa Monkey Bay Assemblies of God m’boma la Mangochi.

Mwambo wa mapemphero umenewu ukuyembekezeka kuyamba nthawi ya 9 koloko m’mawa uno.

President Chakwera ali m’chigawo chaku m’mawa kumene akugwira ntchito zaboma.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Youths should be agents of development — Chithyola-Banda

Romeo Umali

South West Region sees surge in homicide, theft cases

Romeo Umali

IPMM to tackle contemporary HR strategies

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.