Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

President Chakwera akhala nawo pamwambo wa mapemphero

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akhala nawo pa mwambo wa mapemphero pa mpingo wa Monkey Bay Assemblies of God m’boma la Mangochi.

Mwambo wa mapemphero umenewu ukuyembekezeka kuyamba nthawi ya 9 koloko m’mawa uno.

President Chakwera ali m’chigawo chaku m’mawa kumene akugwira ntchito zaboma.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Counterfeit money makers jailed

Romeo Umali

Wanderers Hammered in Mzuzu

Romeo Umali

Government plans to allocate 200,000 hectares for irrigation farming

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.