Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

President Chakwera akhala nawo pamwambo wa mapemphero

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akhala nawo pa mwambo wa mapemphero pa mpingo wa Monkey Bay Assemblies of God m’boma la Mangochi.

Mwambo wa mapemphero umenewu ukuyembekezeka kuyamba nthawi ya 9 koloko m’mawa uno.

President Chakwera ali m’chigawo chaku m’mawa kumene akugwira ntchito zaboma.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Malawi girls develop digital solutions

Romeo Umali

FIRST LADY HAILS MUSLIM WORLD LEAGUE FOR PUMPING K8.5 BN FOR ORPHANS’ EDUCATION SUPPORT

MBC Online

Chakwera arrives in Lusaka ahead of the SADC Extraordinary Summit of Organ Troika

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.