Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

‘Pewani m’chitidwe ogwiritsa ntchito ana’

Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi powaganizira kuti amatuma ana kuti adziwagulitsira malonda nthawi ya sukulu.

Ofalitsa nkhani ku Polisi ya Chileka, a Phillipo Jonathan, anati kutero ndi kuphwanya ufulu wa ana.

A Phillipo anaonjezeranso kuti amanga anthuwo potsatira kuchuluka kwa ana amene amapezeka akugulitsa malonda pa sitolo za ku Lunzu nthawi imene ndi ya sukulu.

Kutsatira izi, apolisi apulumutsa ana 42 ku m’chitidwe umenewu ndipo ena awatumiza kwa makolo awo.

 

Related posts

CFTC tackles contractual matters in Consumer Rights commemoration

Romeo Umali

NASFAM for youth involvement in agriculture

Romeo Umali

Chakwera arrives for MAREP 9 launch at Joho Primary School

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.