Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Majaji agwidwa ndi chisoni ndi imfa ya Kasambara

Majaji m’dziko muno ati ali ndi chisoni kaamba ka imfa ya a Raphael Kasambara omwe anali katswiri wa za malamulo komanso yemwe anathandiza kwambiri polimbikitsa ntchito zamalamulo m’dziko muno.

Justice Zione Ntaba, anena izi pamwambo otsanzikana ndi a Kasambara omwe ukuchitikira kunyumba kwa malemuwa ku Nyambadwe mu mzinda wa Blantyre.

Posachedwapa, maliro apita nawo ku CI komwe kukachitikire mapemphero asananyamule thupi la Malemuwa pa ndege kupita kumudzi kwawo m’boma la Nkhata Bay komwe akaliyike m’manda lolemba.

A Michael Usi, nduna yazosamalira chilengedwe, ndiwo akuimira boma pa mwambowu.

 

Related posts

Support Public Health Services — Daudi

Romeo Umali

Analysts hail Chakwera’s parliamentary engagement on national development

Romeo Umali

YAS tells political parties to include youths in leadership positions

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.