Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Sports Sports

Mzimba Stadium yatsala pang’ono kutha

Adindo a khonsolo ya Mbelwa ati ntchito yomanga bwalo la masewero la Mzimba ikhala ikufika kumapeto pofika m’mwezi wa December chaka chino.

M’modzi mwa akulu akulu a khonsoloyi, a Allan Chitete, ati zambiri zofunikira pa bwalori zinatheka kale.

Bwalo limeneli ndi lokwana anthu 25, 000 ndipo lidzakhalanso ndi ma ofesi amene khonsoloyi idzidzachitira malonda.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Women urged to collaborate for financial independence

MBC Online

A Mwakasungula ati bajeti ili bwino zedi

Blessings Kanache

President Chakwera wafika ku Lilongwe kuchokera ku Blantyre

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.