Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Sports Sports

Mzimba Stadium yatsala pang’ono kutha

Adindo a khonsolo ya Mbelwa ati ntchito yomanga bwalo la masewero la Mzimba ikhala ikufika kumapeto pofika m’mwezi wa December chaka chino.

M’modzi mwa akulu akulu a khonsoloyi, a Allan Chitete, ati zambiri zofunikira pa bwalori zinatheka kale.

Bwalo limeneli ndi lokwana anthu 25, 000 ndipo lidzakhalanso ndi ma ofesi amene khonsoloyi idzidzachitira malonda.

 

Related posts

OYIMBA OMWE ANALI PANSI PA NDE’FEYO AIMBA LERO KU BLANTYRE

Alinafe Mlamba

Boma likufuna kutukula ulimi wa thonje — Kawale

Romeo Umali

Flames eye second spot in World Cup qualifiers

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.