Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Sports Sports

Mzimba Stadium yatsala pang’ono kutha

Adindo a khonsolo ya Mbelwa ati ntchito yomanga bwalo la masewero la Mzimba ikhala ikufika kumapeto pofika m’mwezi wa December chaka chino.

M’modzi mwa akulu akulu a khonsoloyi, a Allan Chitete, ati zambiri zofunikira pa bwalori zinatheka kale.

Bwalo limeneli ndi lokwana anthu 25, 000 ndipo lidzakhalanso ndi ma ofesi amene khonsoloyi idzidzachitira malonda.

 

Related posts

Loans Board approves funding for 28,883 students

Rabson Kondowe

Youths urged to help in building climate resilient societies

MBC Online

Hammers, MAFCO share spoils

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.