Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Malemu Kayanula anali Mlangizi

Mwambo oyankhula pa maliro a malemu Everes Kayanula uli mkati pa bwalo la masewero la Mdika m’mudzi mwa Mtsiro m’boma la Dowa.

Mfumu Mtsiro, Mfumu Simwira ndi oimira banja la Katsukunya ati malemu Kayanula anali mlangizi komanso mlerakhungwa kwa anthu ambiri.

Choncho akubanja komanso mafumu adandaula kaamba ka imfa yao.

Apa, mafumu apempha ana komanso anthu osala kuti azikumbuka kumudzi momwe malemu amachitira.

Malemu Kayanula asiya ana anayi.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Mzuzu Catholic Diocese urges Malawi to seek God’s intervention

MBC Online

MEC plans voter registration ahead of next year’s elections

MBC Online

Chinese enterprises donates 400 bags of maize flour to DoDMA

Yamikani Simutowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.