Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Malemu Kayanula anali Mlangizi

Mwambo oyankhula pa maliro a malemu Everes Kayanula uli mkati pa bwalo la masewero la Mdika m’mudzi mwa Mtsiro m’boma la Dowa.

Mfumu Mtsiro, Mfumu Simwira ndi oimira banja la Katsukunya ati malemu Kayanula anali mlangizi komanso mlerakhungwa kwa anthu ambiri.

Choncho akubanja komanso mafumu adandaula kaamba ka imfa yao.

Apa, mafumu apempha ana komanso anthu osala kuti azikumbuka kumudzi momwe malemu amachitira.

Malemu Kayanula asiya ana anayi.

 

Related posts

Malawi still recording Mpox cases despite high recovery rate

McDonald Chiwayula

BWB secures funding to connect 50,000 new customers

Rabson Kondowe

Livingstonia Synod to plant more than 5 million trees

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.