Malawi Broadcasting Corporation
Development Health Local News Nkhani

Lero ndi tsiku lokumbukira matenda a Fistula

Dziko la Malawi, pamodzi ndi maiko ena onse padziko lapansi, lero akukumbukira tsiku la matenda a kadzamkodzo, amene pachingelezi amatchedwa kuti Fistula.

Tsikuli layamba ndi ulendo wa ndawala ozungulira chipatala cha Bwaila mu mzinda wa Lilongwe pamene anamwino, odwala matendawa komanso adindo ena akuyimba nyimbo komanso kuvina.

Tsikuli amalikumbukira pa 23 May chaka chili chonse pofuna kuwunikira ntchito yolimbana ndi matendawa.

 

Related posts

Min of Justice set to table Judicial Service Administration Bill

Rabson Kondowe

Bullets won’t underestimate Silver — Pasuwa

Romeo Umali

COMESA to launch $25 million facility to accelerate renewable energy transition

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.