Malawi Broadcasting Corporation
Development Health Local News Nkhani

Lero ndi tsiku lokumbukira matenda a Fistula

Dziko la Malawi, pamodzi ndi maiko ena onse padziko lapansi, lero akukumbukira tsiku la matenda a kadzamkodzo, amene pachingelezi amatchedwa kuti Fistula.

Tsikuli layamba ndi ulendo wa ndawala ozungulira chipatala cha Bwaila mu mzinda wa Lilongwe pamene anamwino, odwala matendawa komanso adindo ena akuyimba nyimbo komanso kuvina.

Tsikuli amalikumbukira pa 23 May chaka chili chonse pofuna kuwunikira ntchito yolimbana ndi matendawa.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

NACALA PORT  TO  REDUCE TRANSPORTATION COSTS

MBC Online

Japan to help Malawi eliminate poverty

Rabson Kondowe

Ndimugwetsa ndime yoyamba, Visser achenjeza

Paul Mlowoka
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.