Malawi Broadcasting Corporation
Development Health Local Local News Nkhani

‘Matenda a Kadzamkodzo ndi ochizika’

Banja la bambo ndi mayi Loyd lathokoza chipatala cha boma cha Bwaila chimene chinathandiza mayi Loyd omwe anadwalako matenda a Kadzamkodzo.

Adindo apa chipatalachi adawapatsakonso uphungu komanso zipangizo zoyambira malonda.

Bambo Loyd ati atakumana ndi vutoli, anthu ena adawauza kuti awasiye akazi awo koma iwo adakana mpakana adapeza bwino ndipo chifukwa cha ichi iwo alimbikitsa mabanja ena kuti matendawa ndi ochizika.

Izi zikuchitika pa mwambo okumbukila ntchito yolimbana ndi nthendayi.

 

 

Related posts

Malawi U-21 Korfball Team Beats Zimbabwe 7-3

Yamikani Simtowe

MUST unveils ambitious six-year strategic plan

Romeo Umali

WHO warns against falsified medication

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.