Malawi Broadcasting Corporation
Development Health Local Local News Nkhani

‘Matenda a Kadzamkodzo ndi ochizika’

Banja la bambo ndi mayi Loyd lathokoza chipatala cha boma cha Bwaila chimene chinathandiza mayi Loyd omwe anadwalako matenda a Kadzamkodzo.

Adindo apa chipatalachi adawapatsakonso uphungu komanso zipangizo zoyambira malonda.

Bambo Loyd ati atakumana ndi vutoli, anthu ena adawauza kuti awasiye akazi awo koma iwo adakana mpakana adapeza bwino ndipo chifukwa cha ichi iwo alimbikitsa mabanja ena kuti matendawa ndi ochizika.

Izi zikuchitika pa mwambo okumbukila ntchito yolimbana ndi nthendayi.

 

 

Related posts

Lundu Health Centre calls for support

MBC Online

Takonzeka kuthetsa mbiri ya Bullets — Chimimba

Romeo Umali

Malawi climbs 3rd in World Cup Qualifying group

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.