Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Usi ali ku khonsolo ya Thyolo

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, afika ku ofesi ya Bwanamkubwa wa boma la Thyolo pa ulendo wawo oyendera ntchito za boma mwadzidzidzi.

Iwo afika nthawi itangokwana kota pasiti seveni (7:15) m’mawa uno.

Pakadali pano, DC wa boma la Thyolo, a Hudson Kuphanga, akufotokozera a Usi ntchito zomwe zikugwiridwa m’bomalo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Ophunzira apindilana ndebvu mkamwa

MBC Online

DFIC engages media managers on digital financial services

Stephen Dakalira

TAML, Solidalidad partner to boost women’s roles in tea sector

Arthur Chokhotho
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.