Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Usi ali ku khonsolo ya Thyolo

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, afika ku ofesi ya Bwanamkubwa wa boma la Thyolo pa ulendo wawo oyendera ntchito za boma mwadzidzidzi.

Iwo afika nthawi itangokwana kota pasiti seveni (7:15) m’mawa uno.

Pakadali pano, DC wa boma la Thyolo, a Hudson Kuphanga, akufotokozera a Usi ntchito zomwe zikugwiridwa m’bomalo.

 

Related posts

MAREP Phase 9 on course – Govt

Rabson Kondowe

Bungwe la CHEFO lichilimika kusunga khalidwe

Romeo Umali

Businessman arrested for alleged rape

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.