Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Usi ali ku khonsolo ya Thyolo

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, afika ku ofesi ya Bwanamkubwa wa boma la Thyolo pa ulendo wawo oyendera ntchito za boma mwadzidzidzi.

Iwo afika nthawi itangokwana kota pasiti seveni (7:15) m’mawa uno.

Pakadali pano, DC wa boma la Thyolo, a Hudson Kuphanga, akufotokozera a Usi ntchito zomwe zikugwiridwa m’bomalo.

 

Related posts

Mtukula Pakhomo beneficiaries set to increase in Mzimba

Romeo Umali

MALAWI BROADCASTING CORPORATION EXECUTIVE MANAGEMENT PLACEMENT: DIRECTOR OF NEWS AND CURRENT AFFAIRS

McDonald Chiwayula

CHAKWERA WITHHOLDS ASSENT TO POLITICAL PARTIES (AMENDMENT) BILL; ASSENTS TO 9 OTHERS

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.