Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Dr Usi akhumudwa ndi kuonongwedwa kwa CDF

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi ati ndi okhumudwa kuti ena mwa aphungu anyumba ya malamulo sakuonetsa chidwi chogwiritsa ntchito ndalama zonse zomwe zili mu dongosolo la Community Development Fund (CDF).

Dr Usi amanena izi mu ofesi ya a Bwanamkubwa a m’boma la Thyolo a Hudson Kuphanga.

A Kaphanga amafotokoza kuti zina mwa ndalama zomwe aphunguwa amalandila m’madera a aphungu, sazimvetsa komanso samazigwiritsa ntchito zonse pa chitukuko.

 

Related posts

Govt, parties reflect on governance reforms

Romeo Umali

Sitima yapakati pa LL, BT iyambanso kuyenda — Hara

Romeo Umali

M0626 finale this afternoon

Yamikani Simtowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.