Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Dr Usi akhumudwa ndi kuonongwedwa kwa CDF

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi ati ndi okhumudwa kuti ena mwa aphungu anyumba ya malamulo sakuonetsa chidwi chogwiritsa ntchito ndalama zonse zomwe zili mu dongosolo la Community Development Fund (CDF).

Dr Usi amanena izi mu ofesi ya a Bwanamkubwa a m’boma la Thyolo a Hudson Kuphanga.

A Kaphanga amafotokoza kuti zina mwa ndalama zomwe aphunguwa amalandila m’madera a aphungu, sazimvetsa komanso samazigwiritsa ntchito zonse pa chitukuko.

 

Related posts

Ntcheu North MP urges constituents to register for 2024 elections

Romeo Umali

‘Kukwinimbira ndi vuto lalikulu m’Malawi’

Romeo Umali

Chakwera reveals ambitious plan for cervical cancer centres

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.