Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Dr Usi akhazikitsa nawo Malawi Church and Community Transformation Movement

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi ali nawo pa zochitika zokhazikitsa bungwe la Malawi Church and Community Transformation Movement m’chigawo cha kum’mwera.

Bungweli ndi lopangidwa ndi atsogoleri amipingo ndipo lidzigwira ntchito ndi mafumu komanso anthu osiyanasiyana.

Cholinga chake ndi kulimbikitsa ntchito zabwino m’magawo osiyanasiyana a chitukuko.

Dr Usi anayenda nawo pa ulendo wa ndawala kuchoka ku HHI mpakana pa mpingo wa Word Alive International Ministries munzinda wa Blantyre.

 

Related posts

Chakwera akutsegulira ntchito ya Millennium Challenge Corporation yokonza misewu

Rabson Kondowe

LCC pledges to reunite street connected children with their families

Alinafe Mlamba

Treasury lauds Standard Bank for innovative, customer centred principles

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.