Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Dr Usi akhazikitsa nawo Malawi Church and Community Transformation Movement

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi ali nawo pa zochitika zokhazikitsa bungwe la Malawi Church and Community Transformation Movement m’chigawo cha kum’mwera.

Bungweli ndi lopangidwa ndi atsogoleri amipingo ndipo lidzigwira ntchito ndi mafumu komanso anthu osiyanasiyana.

Cholinga chake ndi kulimbikitsa ntchito zabwino m’magawo osiyanasiyana a chitukuko.

Dr Usi anayenda nawo pa ulendo wa ndawala kuchoka ku HHI mpakana pa mpingo wa Word Alive International Ministries munzinda wa Blantyre.

 

Related posts

Kulimbikitsa ngodya zisanu zamaphunziro

Rabson Kondowe

Ulumali si kulephera — Papkid

Romeo Umali

More than 70,000 registered in NRB exercise

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.