Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Dr Usi akhazikitsa nawo Malawi Church and Community Transformation Movement

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi ali nawo pa zochitika zokhazikitsa bungwe la Malawi Church and Community Transformation Movement m’chigawo cha kum’mwera.

Bungweli ndi lopangidwa ndi atsogoleri amipingo ndipo lidzigwira ntchito ndi mafumu komanso anthu osiyanasiyana.

Cholinga chake ndi kulimbikitsa ntchito zabwino m’magawo osiyanasiyana a chitukuko.

Dr Usi anayenda nawo pa ulendo wa ndawala kuchoka ku HHI mpakana pa mpingo wa Word Alive International Ministries munzinda wa Blantyre.

 

Related posts

MCC launches Reading Glasses for Improved Livelihoods Programme

Yamikani Simtowe

DAPP donates refuse bins to Lilongwe City Council

Rabson Kondowe

Mwana wamwalira makolo ake atakana kumutengera kuchipatala

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.