Malawi Broadcasting Corporation
Business Local News Nkhani

Chakumwa chaukali chatsopano!

Kampani yofulula mowa ya Castel, yakhazikitsa chakumwa chatsopano chimene akuchitcha kuti Pomme Breeze.

M’modzi mwa akuluakulu a kampaniyi, a Fiona Nyambo, ati chakumwa chaukali chimenechi ndi chozuna komanso chokonzedwa mwa makono.

 

Related posts

SERIAL OFFENDER APPREHENDED FOR BURGLARY, THEFT IN MONKEY-BAY

Romeo Umali

Kalembetseni m’kaundula wa MEC kuti mudzavote — MCP

Romeo Umali

A Chakwera alibe tsankho — Chimwendo Banda

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.