Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

A Mnjale amwalira

Yemwe anaakhalapo mkulu wa nthambi ya CID, a George Mnjale, amwalira lero ku chipatala cha Kamuzu Central mumzinda wa Lilongwe kumene amalandira thandizo.

A Mnjale amwalira ali pa udindo wa wachiwiri kwa komishonala wa apolisi (Deputy Commissioner of Police).

Iwo anabadwa pa 24 October, 1970 ndipo amachokera m’boma la Dowa.

#MBCDigital
#Manthu

Print Friendly, PDF & Email

Author

  • Mayeso Chikhadzula joined MBC in 2006, he's an Investigative Journalist and Principal Reporter. He's also a News Anchor, Presenter, and producer.

Related posts

Bravehearts dominate CEZOBAL with 6th title in a row

MBC Online

Tsopano ndikupeza bwino-Ras Kansengwa

Amugwira chifukwa chotentha manja a mwana wake

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.