Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

A Mnjale amwalira

Yemwe anaakhalapo mkulu wa nthambi ya CID, a George Mnjale, amwalira lero ku chipatala cha Kamuzu Central mumzinda wa Lilongwe kumene amalandira thandizo.

A Mnjale amwalira ali pa udindo wa wachiwiri kwa komishonala wa apolisi (Deputy Commissioner of Police).

Iwo anabadwa pa 24 October, 1970 ndipo amachokera m’boma la Dowa.

#MBCDigital
#Manthu

Related posts

‘AMalawi adzipindula ndi zachikhalidwe’

Romeo Umali

LUANAR signs MOU with Astria Learning

Rabson Kondowe

Culture can help achieve Malawi 2063

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.