Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

A Chakwera ali mu mzinda wa Mzuzu

Prezidenti Dr Lazarus Chakwera wauza anthu amchigawo chakumpoto kuti boma lake ladzipereka potukula miyoyo ya anthu mdziko muno kudzanso mchigawochi.

Dr Chakwera amalankhula pa Katoto mu mzinda wa Mzuzu pofika mchigawochi komwe khwimbi linasonkhana pomulandira.

Mtsogoleriyu wapemphanso anthu mdziko muno kuti alimbikitse umodzi.

Related posts

Ulumali si kulephera — Papkid

Romeo Umali

GEFT ichepetsa mavuto obwera ndi kusintha kwa nyengo — Boma, UNDP

Romeo Umali

A Bango ayamika Dr Chakwera chifukwa choganizira anthu a m’boma la Kasungu

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.