Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

A Chakwera ali mu mzinda wa Mzuzu

Prezidenti Dr Lazarus Chakwera wauza anthu amchigawo chakumpoto kuti boma lake ladzipereka potukula miyoyo ya anthu mdziko muno kudzanso mchigawochi.

Dr Chakwera amalankhula pa Katoto mu mzinda wa Mzuzu pofika mchigawochi komwe khwimbi linasonkhana pomulandira.

Mtsogoleriyu wapemphanso anthu mdziko muno kuti alimbikitse umodzi.

Related posts

Anthu akukhamukira kumwambo wa Chikumbutso ku Mulanje

Romeo Umali

Anthu aku Mangochi akondwa ndi kusindikiza zitupa zoyendera

Rabson Kondowe

Tipitiriza kuthandiza Malawi – IMF

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.