Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

A Chakwera ali mu mzinda wa Mzuzu

Prezidenti Dr Lazarus Chakwera wauza anthu amchigawo chakumpoto kuti boma lake ladzipereka potukula miyoyo ya anthu mdziko muno kudzanso mchigawochi.

Dr Chakwera amalankhula pa Katoto mu mzinda wa Mzuzu pofika mchigawochi komwe khwimbi linasonkhana pomulandira.

Mtsogoleriyu wapemphanso anthu mdziko muno kuti alimbikitse umodzi.

Related posts

Olemba nkhani awalangiza kuti afalitse nkhani zokhudza matenda a nkhawa ndi muubongo

MBC Online

Dr Chakwera apereka K5 million zothandizira pamaliro a Kasambara

Chisomo Manda

‘Malamulo a chipani akuvomereza atosgoleri ake kudzachita mgwirizano ndizipani zina’

Yamikani Simtowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.