Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Anthu akukhamukira kumwambo wa Chikumbutso ku Mulanje

Khwimbi la anthu likukhamukira ku bwalo la zamasewero la Mulanje kumene kukhale mwambo wokumbukira kuti patha chaka chimodzi chichitikireni Namondwe wa Freddy.

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, ndiye atsogolere nwambowu komwe kwafika kale anthu osiyanasiyana, kuphatikizapo mafumundi akuluakulu ena.

Olemba : Blessings Cheleuka

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

USA ANNOUNCES K158 BILLION SUPPORT TO MALAWI

MBC Online

CHAKWERA OPENS K30 BN PHALOMBE HOSPITAL

Blessings Kanache

MAN NABBED FOR BURGLARY, POLICE RECOVER K10 MN

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.