Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Anthu akukhamukira kumwambo wa Chikumbutso ku Mulanje

Khwimbi la anthu likukhamukira ku bwalo la zamasewero la Mulanje kumene kukhale mwambo wokumbukira kuti patha chaka chimodzi chichitikireni Namondwe wa Freddy.

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, ndiye atsogolere nwambowu komwe kwafika kale anthu osiyanasiyana, kuphatikizapo mafumundi akuluakulu ena.

Olemba : Blessings Cheleuka

Related posts

Chaka chatha chichitikireni Namondwe Freddy

Romeo Umali

British Govt reaffirms support for meteorological services

Romeo Umali

South West Region records drop in crime rate

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.