Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Anthu akukhamukira kumwambo wa Chikumbutso ku Mulanje

Khwimbi la anthu likukhamukira ku bwalo la zamasewero la Mulanje kumene kukhale mwambo wokumbukira kuti patha chaka chimodzi chichitikireni Namondwe wa Freddy.

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, ndiye atsogolere nwambowu komwe kwafika kale anthu osiyanasiyana, kuphatikizapo mafumundi akuluakulu ena.

Olemba : Blessings Cheleuka

Related posts

Chakwera urges UN for more support, hails cordial working relationship

Mayeso Chikhadzula

Malawi aligns with global ethical AI standards

McDonald Chiwayula

All set for Wazisomo Thank You Concert

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.