Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Manja SDA ikutsekera msonkhano wa Misasa

Mpingo wa Manja Seventh Day Adventist mu nzinda wa Blantyre lero ukumalizitsa msonkhano wake wa pachaka wa Misasa omwe unayamba pa 27 August 2024.

Mutu wa msonkhanowu ndi ‘Kusandulika mu chikhalidwe pomwe tikukatumikira’.

Mlaliki wa mkulu pa msonkhanowu ndi mtsogoleri wakale wa Seventh Day Adventist m’dziko muno, abusa Frackson Kuyama.

Mu ulaliki wawo iwo anayamba ndi kulangiza akhristu kuti adzikhala ololerana posasungirana mangawa, kukhala okhutira ndi zomwe ali nazo komanso kusamalira chakudya.

 

Related posts

Farmers in Kasungu embrace crop diversification for better yields

MBC Online

Pulezidenti wakale wa FAMA wafunira zabwino Mayi Kingston

Romeo Umali

MEC impressed with voter turn-out

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.