Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Anyamata awiri anjatidwa ataba katundu wa K500,000

Apolisi m’boma la Mangochi amanga a Rashid Mailosi a zaka 18 ndi a Paul Edward a zaka 19 powaganizira kuti anathyola nyumba yogulitsira katundu ndi kubamo katundu wandalama pafupifupi K500,000.

Ofalitsa nkhani pa polisi ya Mangochi, Amina Tepani Daudi, watsimikiza nkhaniyi ndipo wati awiriwa akaonekera kubwalo lamilandu kukayankha mulandu wakuba.

 

Related posts

Kyungu urges transparency and accountability among duty bearers

Rabson Kondowe

Man Gets 12 Years IHL for Defilement

Alick Sambo

Madotolo okonza nkhope za anthu afika

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.