Malawi Broadcasting Corporation
Education Local Local News Nkhani

Emmanuel University idziphunzitsa Kiswahili

Sukulu ya ukachenjede ya Emmanuel imene ndi ya mu mnzinda wa Lilongwe yalengeza zoyamba kuphunzitsa Kiswahili ngati phunziro lapadera.

Izi zadziwika pa mwambo okondwelera chilankhulochi kumene kuli kazembe wa dziko lino mayi Agnes Kayola amene akuyembekeza mtsogoleri wa dziko la Tanzania mayi Samia Suluhu Hassan kuti achite zoyankhula kudzera pa uthenga wa pa kanema.

Pa malo amene pakuchitikira mwambowu pakuyankhulidwa ziyankhulo za Kiswahili, Chichewa ndi Chingerezi.

 

Related posts

Govt to enhance quality learning

MBC Online

Chisale’s intimidation case ruling shifted

Romeo Umali

Maize prices drop in September

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.