Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Dr Chakwera apereka K5 million zothandizira pamaliro a Kasambara

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera wapereka ndalama zokwana K5 million kuti zithandizire pamwambo wa maliro a Raphael Kasambara omwe atisiya masiku apitawa.

A Harry Mkandawire, amene akuyimira Dr Chakwera, ati malemu a Raphael Kasambara anali munthu okonda kumenyera ufulu wa anthu osauka.

Iwo ati boma lisowa ntchito zambiri zomwe malemuwa anathandizirapo maaka pa chitukuko.

A Mkandawrire ayankhula izi pamene mwambo wa maliro uli mkati m’boma la Nkhata Bay.

Related posts

Ochita bwino muligi ya CRNL adzilandira K50,000 sabata iliyonse

Rabson Kondowe

Timu ya Hilltop Socials yawina chikho cha under 21 ku Mzuzu

Alinafe Mlamba

Deposit Insurance Corporation ayikhazikitsa sabata lamawa

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.