Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Politics

Nancholi yayankhula

Kuli khwimbi la undipondera mwana pa bwalo la Nancholi mu mzinda wa Blantyre pamene mtsogoleri wakale wa dziko llino Dr Joyce Banda akuchititsa msonkhano.

A George Nnesa, omwe ndi mtsogoleri wa chipani cha Mafunde, nawo alinso pa msonkhanowu.

Padakali pano, a Noah Chimpeni ndi amene akuchita zoyankhula pamene akulandila akulu akulu amene anali ku chipani chotsutsa cha DPP ku chipani cha PP.

Olemba : Blessings Cheleuka

#MBCDigital
#Manthu

Related posts

CIVIL SOCIETY WEIGHS IN ON KAPONDAMGAGA’S REINSTATEMENT

MBC Online

CSOs bang heads on Social Protection Programmes

Alinafe Mlamba

NICO Group launches One NICO Lived Experience

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.