Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

A Mnjale amwalira

Yemwe anaakhalapo mkulu wa nthambi ya CID, a George Mnjale, amwalira lero ku chipatala cha Kamuzu Central mumzinda wa Lilongwe kumene amalandira thandizo.

A Mnjale amwalira ali pa udindo wa wachiwiri kwa komishonala wa apolisi (Deputy Commissioner of Police).

Iwo anabadwa pa 24 October, 1970 ndipo amachokera m’boma la Dowa.

#MBCDigital
#Manthu

Related posts

IMF APPROVES RCF FOR MALAWI

McDonald Chiwayula

‘Andale asamalowelere ntchito zam’ma khonsolo’

Alinafe Mlamba

OPERATION USALAMA SWEEPS STREET – CONNECTED CHILDREN IN BLANTYRE

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.