Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Prezidenti Chakwera akhala nawo pa mwambo operekeza maliro

Anthu ochuluka asonkhana ku nyumba ya chisoni ya Sunset Funeral Services ku Kanengo munzinda wa Lilongwe komwe pali chikonzero chonyamula ena mwa matupi a anthu omwe adafa pangozi ya ndege limodzi ndi wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, malemu Dr Saulos Chilima.

Pali chiyembekezo choti pa mwambowu pakhalanso mwambo wa Misa poremekeza mzimu wa mayi Patricia Shanil Dzimbiri, omwe anaakhalapo mayi wa dziko lino zaka za mmbuyomu.

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, komanso mayi wa dziko lino, Madam Monica Chakwera, akuyembekezeka kukhala nawo pamwambowu.

 

Print Friendly, PDF & Email

Author

  • Mayeso Chikhadzula joined MBC in 2006, he's an Investigative Journalist and Principal Reporter. He's also a News Anchor, Presenter, and producer.

Related posts

“Let’s work together in revolutionizing the Agriculture sector”

MBC Online

Tay Grin among the headliners of this year’s Kumingoli Bash

Emmanuel Chikonso

First Lady in Geneva for TB Summit

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.