Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Tourism

President Chakwera ayendera ntchito zachitukuko ku Mangochi

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera m’mawa uno ali pa ulendo oyendera ntchito zachitukuko m’boma la Mangochi.

Dr Chakwera akuyembekezeka kuyendera komanso kucheza ndi anthu ogwira ntchito zokopa alendo ndipo ena mwa malowa ndi a Rosalyn’s Beach Hotel.

Dr Chakwera ayenderanso kampani yopanga cement ya Cement Products Limited ku Njereza ndipo akatero akayendera malo antchito zokopa alendo a Club Makokola komwenso akacheze ndi ogwira ntchito zamalonda.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Abambo ambiri siali pa ndondomeko yama ARV — Nyirenda

Romeo Umali

Kayerekera Uranium Mine rollout excites govt

Mayeso Chikhadzula

Alimi apempha Dr Chakwera kuti awathandize kupeza misika mosavuta

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.