Malawi Broadcasting Corporation
International News Nkhani

Ndege ya Russia ayipeza

Zidutswa za ndege imene inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazhets m’dziko la Russia azipeza.

Malinga ndi unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dzikolo, anthu 17 afa pa ngoziyi ndipo ena asanu sanawapeze.

Ndegeyi inanyamula anthu 22.

Padakali pano, ntchito yoyang’ana anthu amene sanawapeze idakali mkati.

Olemba: Alufisha Fischer

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

SADC has lost an important leader —Chakwera

Eunice Ndhlovu

Kuphunzira m’magulu kuli ndi phindu

Lonjezo Msodoka

Ukayidi wa zaka zitatu ataba ng’ombe ya Eid

Charles Pensulo
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.