Malawi Broadcasting Corporation
International News Nkhani

Ndege ya Russia ayipeza

Zidutswa za ndege imene inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazhets m’dziko la Russia azipeza.

Malinga ndi unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dzikolo, anthu 17 afa pa ngoziyi ndipo ena asanu sanawapeze.

Ndegeyi inanyamula anthu 22.

Padakali pano, ntchito yoyang’ana anthu amene sanawapeze idakali mkati.

Olemba: Alufisha Fischer

Related posts

MCM emphasises ethical standards

Alinafe Mlamba

JENDA POLICE APPREHEND 5 NOTORIOUS THIEVES

Romeo Umali

MRA drone border patrols to save billions

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.