Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Mwezi sunaoneke, tchuthi lachinayi —MAM

Bungwe la asilamu la Muslim Association of Malawi (MAM) lati mwezi otsiriza kusala kudya wa Ramadan sunaoneke, choncho iwo ati Eid idzakhalapo lachinayi.

Mneneri wa bungweli, Sheikh Dinala Chabulika, auza MBC kuti zateremu ndiye kuti asilamu atsiriza kusala kudya mawa lachitatu ndipo tchuthi cha Eid chidzachitika lachinayi likudzali.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

2024 JCE exams start on a positive note

Madalitso Mhango.

Aliyense apindula ndi ntchito zachitukuko cha boma- Chimwendo Banda

Alinafe Mlamba

NEW CFTC BOSS PROMISES TO END CARTELS

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.