Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Mwezi sunaoneke, tchuthi lachinayi —MAM

Bungwe la asilamu la Muslim Association of Malawi (MAM) lati mwezi otsiriza kusala kudya wa Ramadan sunaoneke, choncho iwo ati Eid idzakhalapo lachinayi.

Mneneri wa bungweli, Sheikh Dinala Chabulika, auza MBC kuti zateremu ndiye kuti asilamu atsiriza kusala kudya mawa lachitatu ndipo tchuthi cha Eid chidzachitika lachinayi likudzali.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Dr Chakwera wabwelera ku Lilongwe

MBC Online

Government says vocational training crucial as 750 graduate

Steve Dakalira

WVM bails out hunger affected households in Chikwawa

Charles Pensulo
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.