Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Mgwirizano wamaulendo apa madzi watheka

Dziko la Malawi lasayinira mgwirizano ndi kampani zomwe zimapanga komanso kuyendetsa ntchito za sitima za pamadzi kuti zidzayambitse ntchitoyi pa nyanja ya Malawi.

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, komanso nduna ya zamtengatenga, a Jacob Hara, ndi amene asayina mgwirizanowu m’malo mwa boma la Malawi.

Kampanizi zalonjeza zobwera ku Malawi posachedwa, mogwirizana ndi pempho la Dr Chakwera kuti athetse mavuto amaulendo apamadzi pa nyanja ya Malawi.

Mwambowu unachitikira munzinda wa Frankfurt m’dziko la Germany mu imodzi mwa sitima ya pamadzi zomwe amapanga m’dziko la German

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Silver Strikers near unbeaten first round

MBC Online

BWALO LA MILANDU LABWEZA GALIMOTO YA UMBONI WABOMA

MBC Online

Anthu a ku Ntcheu ndiwothokoza – Nyakwawa Gwedeza

Justin Mkweu
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.