Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Politics

Tiyeni tipitirize kumvera mtsogoleri komanso kukonda chipani chathu — Msukwa

Wapampando wa komiti yomwe yakonza msonkhano waukulu wa chipani cha Malawi Congress a Kezzie Msukwa walangiza mamembala a chipanichi kuti apitirize kukhala pambuyo pa Prezidenti Dr Lazarus Chakwera, yemwenso ndi mtsogoleri wa chipanichi.

A Msukwa alangizanso mamembala a chipanichi kuti apitirize kusunga mwambo mchipani komanso kumvera mtsogoleri wa chipanichi.

Iwo ati ali ndi chikhulupiliro kuti chipani cha MCP chidzapambana pa chisankho cha chaka chamawa.

Olemba: Isaac Jali ndi Olive Phiri

Related posts

Shop Manager jailed for 11 years over theft, arson

Romeo Umali

Dr Chakwera to attend late Reverend Mgawi’s funeral

MBC Online

Alandira mphotho ya galimoto

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.