Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Mwambo wa maliro wa malemu Kayanula wayamba

Mwambo oona nkhope ya muulutsi wakale pa wayilesi ya MBC, malemu Everes Kayanula, tsopano uli nkati kumudzi kwao kwa Mtsiro mfumu yaikulu Kayembe m’boma la Dowa.

Malemu Kayanula anamwalira pa 5 July mwezi uno mu nzinda wa Blantyre.

Agwira ntchito youlutsa mau kwa zaka 35 ndipo anapuma pantchito mchaka cha 2018.

 

Related posts

Mpingo wa CCAP walandira a Moses Kunkuyu m’gulu la Utumiki wa Abambo

Rabson Kondowe

Lilongwe businessman wins big in BetPawa’s aviator

MBC Online

Increased digital banking uptake key to paperless transactions

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.