Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Mlimi watola chikwama

Mlimi wa ku Blantyre, a Mariko Kalima, wayiphula pamene wapata K2.5 million mu mpikisano wa Tisanje umene ikupangitsa ndi kampani yopanga sopo ya Hirwa General Dealers.

Polankhula pamene kampaniyi imapereka mphothoyi ku Ndirande munzinda wa Blantyre, kudzera kwa kazembe wawo, Emmie Deebo, a Kalima anathokoza kampaniyi ponena kuti ndalama iwathandiza pogula fetereza ndi zipangizo zina za kumunda.

Mkulu owona za malonda ku kampaniyi, a Best Balala, anati anakhazikitsa mpikisanowu pofuna kuthandiza makasitomala awo mu nthawi ino pamene chuma chikuvuta.

Related posts

Ntchisi CS-EPWP participants hail timely payment

Romeo Umali

Stage set for new TNM sponsorship package

Romeo Umali

Malawi in COSAFA Beach Soccer Group A

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.